Love the sinner - Emmax

Love the sinner - Emmax

  • Year of release: 2021
  • Language: English
  • Duration: 3:25

Below is the lyrics of the song Love the sinner , artist - Emmax with translation

Lyrics " Love the sinner "

Original text with translation

Love the sinner

Emmax

Verse 1- Mic Mash

Anzanga omwe ndimacheza nawo

Zoti kuli yesu they should know now

Achristu amatijaja tikamadya ndi anthu ochimwa

Anayamba ndi yesu nde sitikuti tikuchimwa

Amati tisamakhale ndi anthu otayika

Samadziwa kuti tikumanga alter yi ka

Asintha bwanji anthu ngati ifeyo tikuwasala

Tiwalalikile yehovah akabwela sadzatsala

We judge others because of the way they sin different

Ulibe tchimo ponya mwala if you’re so perfect

A lot of believers are self-righteous, lost focus like object is close to the

eye

Mumathila anzanu khonko muti zadziko ayi

Lie, we are so divided like a pie

Why?

Eveytime we want to be so high

Jesus is for everybody si wa simoko ngati brai

We have gay friends, lesbians, drunkard etc

We point fingers tikaona osochela

Ma hule, akuba, akupha etc

They need Jesus ife timawatsekela

Who lied to you kuthoka ndi martse uyamba mwano?

The world is scary koma ndiyesu sungathele pano

Pray that you don’t fall go

Into the world and preach the gospel this is the goal

Hook — Emmax

He came for the sinners, broken hearted and the lost (yeahhh)

For the weak and the troubled and he paid the cost (paid the cost)

For the fornicators, tax evaders, poor or boss, (yeahhh)

For them all.

And he nailed it to a cross (to a cross)

If you of God, you gone reach the whole world (whole world)

To sinner or free you gatto preach the gospel (gospel)

How they gone know Christ without showing love (love)

How they gone know truth without showing God

Verse 2- Mic Mash

Aroma verse ya 11 ndime 10

Ngati zadziko zili tsitsi ndimeteni

You’ll never put me to shame ine ndiwanu servant

Kwathu sipadziko pansi pano ine ndiwa rent

Ambiri ondizungulira ndafalisi

A christu apagulu nthawi zonse they do criticise

In your word you never specified, Go into the world and preach you didn’t put

us in a box

I don’t want to live like a hypocrite

Lord i know I’m not perfect

Ndifalitse uthengawu mu street

Zolalika kwama B. A okhazi sizoona

Train me ooh God ndinu njanji oona

This life of mine you’re the owner

Ndimukonde ochimwa tate koma ndidane ndi machimo

Kuwedza modzi the Joy in heaven is so much more

New texts and translations on the site:

2+ million lyrics

Songs in different languages

Translations

High-quality translations into all languages

Quick search

Find the texts you need in seconds